29/12/2025
Tumiki wa Allah Muhammad ο·Ί adat { akakhala kuti muthuyo ali wazintchito zoyipa pamene geneza yanyamulidwa ndikuyikidwa paphewa wakufayo amati inu ine mozi mwayinu mukunditengela kuti ndipo mawu awawa amaveka kucholengedwa chilichose cha Allah kupatula muthu . .
{ Bukhar 1314}
Ndipo muthawi iyiyi ali muthu oti amachita zabwino sadandaula kathu ndipo amawonaso kuchedwa kukamusiya kumandako .
Ndisiku lamasawuso wallah kwa anthu ochulusa kucheza paduniya . Zipulumuseni nokha pachomwe chikuza.
Khalan ndizelu pozizindikila kuti umoyo ndili nawo ndiwokhala pangβono .
Tizipepha Allah kuti imfa izatipeze tili ayiman ameen